Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 49:19 - Buku Lopatulika

Ndi Gadi, achifwamba adzampsinja iye; koma iye adzapsinja pa chitendeni chao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi Gadi, achifwamba adzampsinja iye; koma iye adzapsinja pa chitende chao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Gadi anthu achifwamba adzamthira nkhondo, koma iyeyo adzaŵatembenukira nkuŵapirikitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Gadi adzachitidwa chiwembu ndi gulu la amaliwongo, koma iye adzawathamangitsa.

Onani mutuwo



Genesis 49:19
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi.


Ndi ana aamuna a Gadi: Zifiyoni, ndi Hagi, ndi Suni, ndi Eziboni, ndi Eri, ndi Arodi, ndi Areli.


Ndi Asere, chakudya chake ndicho mafuta, ndipo adzapereka zolongosoka zachifumu.


Ezere mkulu wao, wachiwiri Obadiya, wachitatu Eliyabu,


Ndipo Mulungu wa Israele anautsa mzimu wa Pulo mfumu ya Asiriya, ndi mzimu wa Tigilati-Pilesere mfumu ya Asiriya, ndiye anawatenga ndende; ndiwo Arubeni, ndi Agadi, ndi hafu la fuko la Manase, nafika nao ku Hala, ndi Habori, ndi Hara ndi ku mtsinje wa Gozani, mpaka lero lino.


Pamodzi ndi iye Arubeni ndi Agadi analandira cholowa chao, chimene Mose adawapatsa tsidya ilo la Yordani kum'mawa, monga Mose mtumiki wa Yehova anawapatsa;