Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 49:13 - Buku Lopatulika

Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Zebuloni adzakhala m'mbali mwa nyanja, madooko ake adzakhala malo a zombo, dziko lake lidzafika mpaka ku Sidoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Zebuloni adzakhala mʼmphepete mwa nyanja; adzakhala pa dooko la sitima zapamadzi; malire ake adzafika ku Sidoni.

Onani mutuwo



Genesis 49:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Mulungu anandipatsa ine mphatso yabwino; tsopano mwamuna wanga adzakhala ndi ine, chifukwa ndambalira iye ana aamuna asanu ndi mmodzi; ndipo anamutcha dzina lake Zebuloni.


Maso ake adzafiira ndi vinyo, ndipo mano ake adzayera ndi mkaka.