Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 49:12 - Buku Lopatulika

Maso ake adzafiira ndi vinyo, ndipo mano ake adzayera ndi mkaka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Maso ake adzafiira ndi vinyo, ndipo mano ake adzayera ndi mkaka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maso ake ndi ofiira ndi vinyo mano ake ndi oyera ndi mkaka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Maso ake adzakhala akuda chifukwa cha vinyo, mano ake woyera chifukwa cha mkaka.

Onani mutuwo



Genesis 49:12
3 Mawu Ofanana  

Adamanga mwana wa kavalo wake pampesa, ndi mwana wa bulu wake pa mpesa wosankhika; natsuka malaya ake m'vinyo, ndi chofunda chake m'mwazi wa mphesa.


Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.


Ndani ali ndi chisoni? Ndani asauka? Ndani ali ndi makangano? Ndani ang'ung'udza? Ndani alasidwa chabe? Ndani afiira maso?