Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 47:2 - Buku Lopatulika

Ndipo mwa abale ake anatengako anthu asanu, nawaonetsa iwo kwa Farao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mwa abale ake anatengako anthu asanu, nawaonetsa iwo kwa Farao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aŵa ndi asanu mwa abale angawo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anapita kwa Farao kuja ndi abale ake asanu, kukawaonetsa.

Onani mutuwo



Genesis 47:2
5 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala pamene Farao adzaitana inu, nadzati, Ntchito yanu njotani?


Ndipo pa ulendo wachiwiri Yosefe anazindikirika ndi abale ake; ndipo fuko la Yosefe linaonekera kwa Farao.


podziwa kuti Iye amene anaukitsa Ambuye Yesu adzaukitsa ifenso pamodzi ndi Yesu, nadzatiikapo pamodzi ndi inu.


amene timlalikira ife, ndi kuchenjeza munthu aliyense ndi kuphunzitsa munthu aliyense mu nzeru zonse, kuti tionetsere munthu aliyense wamphumphu mwa Khristu;


Ndipo kwa Iye amene akhoza kukudikirani mungakhumudwe, ndi kukuimikani pamaso pa ulemerero wake opanda chilema m'kukondwera,