Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 45:25 - Buku Lopatulika

Ndipo anakwera kutuluka mu Ejipito, nafika ku dziko la Kanani kwa Yakobo atate wao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anakwera kutuluka m'Ejipito, nafika ku dziko la Kanani kwa Yakobo atate wao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono iwo adachoka ku Ejipito, kubwerera ku Kanani kwa bambo wao Yakobe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anachoka ku Igupto nafika kwa abambo awo Yakobo mʼdziko la Kanaani.

Onani mutuwo



Genesis 45:25
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo;


Ndipo anamukitsa abale ake, ndipo anachoka; ndipo anati kwa iwo, Musakangane panjira.


Ndipo anamfotokozera iye kuti, Yosefe akali ndi moyo, ndipo alamulira m'dziko lonse la Ejipito. Pamenepo mtima wake unakomoka, pakuti sanawakhulupirire iwo.