Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 44:6 - Buku Lopatulika

Ndipo anapeza iwo, nanena nao mau omwewo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapeza iwo, nanena nao mau omwewo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wantchito uja ataŵapeza, adanena mau omwe adaamuuza aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wantchito uja atawapeza ananena mawu anawuzidwa aja.

Onani mutuwo



Genesis 44:6
3 Mawu Ofanana  

Kodi si ndicho chomwera nacho mbuyanga, naombeza ula nacho? Mwachitira choipa pakutero.


Nati kwa iye, Bwanji mbuyanga anena mau otere? Ngati nkutheka kuti akapolo anu achite chotero?


Pakuti, taonani, ichi chomwe, chakuti mudamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, khama lalikulu lanji chidalichita mwa inu, komanso chodzikonza, komanso mkwiyo, komanso mantha, komanso kukhumbitsa komanso changu, komanso kubwezera chilango! M'zonse munadzitsimikizira nokha kuti muli oyera mtima m'menemo.