Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 44:3 - Buku Lopatulika

Pamene kudacha, anamukitsa anthu iwo ndi abulu ao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene kudacha, anamukitsa anthu iwo ndi abulu ao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa kutacha, anthu aja adaloledwa kupita pamodzi ndi abulu ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmawa kutacha anthu aja analoledwa kuti apite ndi abulu awo.

Onani mutuwo



Genesis 44:3
2 Mawu Ofanana  

Nuike chikho changa, chikho chasiliva chija, kukamwa kwa thumba la wamng'ono, pamodzi ndi ndalama za tirigu zake. Ndipo iye anachita monga mau ananena Yosefe.


Atatuluka m'mzinda asanamuke patali, Yosefe anati kwa tsanyumba wake, Tanyamuka, talondola anthu aja, ukawapeza unene nao, Chifukwa chanji mwabwezera zoipa m'malo mwa zabwino?