Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 44:11 - Buku Lopatulika

Ndipo anafulumira natsitsa pansi yense thumba lake, namasula yense thumba lake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anafulumira natsitsa pansi yense thumba lake, namasula yense thumba lake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero onsewo adatsitsa msanga matumba ao, aliyense nkumasula thumba lake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono onse anafulumira kutsitsa pansi aliyense thumba lake ndi kulitsekula.

Onani mutuwo



Genesis 44:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene wina wa iwo anamasula thumba lake kuti adyetse bulu wake pachigono, anapeza ndalama zake; taonani, zinali kukamwa kwa thumba lake.


Ndipo iye anati, Tsononso chikhale monga mwa mau anu: iye amene ampeza nacho adzakhala kapolo wanga; ndipo inu mudzakhala opanda chifukwa.


Ndipo iye anafunafuna kuyambira pa wamkulu naleka pa wamng'ono nachipeza chikho m'thumba la Benjamini: