Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 43:20 - Buku Lopatulika

Mfumu, tinatsikira ndithu nthawi yoyamba kudzagula chakudya:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mfumu, tinatsikira ndithu nthawi yoyamba kudzagula chakudya:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

namuuza kuti, “Pepani bwana, ife tidaabweranso kuno kale kudzagula chakudya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Pepani mbuye wathu, ife tinabweranso ulendo woyamba kudzagula chakudya

Onani mutuwo



Genesis 43:20
9 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anati kwa iye, Iai, mbuyanga, koma akapolo anu adzera kudzagula chakudya.


Ndipo pamene wina wa iwo anamasula thumba lake kuti adyetse bulu wake pachigono, anapeza ndalama zake; taonani, zinali kukamwa kwa thumba lake.


Ndipo abale ake a Yosefe khumi anatsikira kukagula tirigu mu Ejipito.


Ndipo panali pamene analikukhuthula matumba ao, taonani, phukusi la ndalama la yense linali m'thumba lake; ndipo pamene iwo ndi atate ao anaona mapukusi a ndalama anaopa.


Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati,


ndipo panali pamene ife tinafika pachigono, tinamasula matumba athu, ndipo taonani ndalama za yense zinali kukamwa kwa thumba lake, ndalama zathu mkulemera kwake; ndipo tabwera nazo m'manja mwathu.


Ndipo Yuda ananena ndi iye kuti, Munthu uja anatilimbitsira mau kuti, simudzaonanso nkhope yanga, koma mphwanu akhale ndi inu ndiko.


Ndipo iwo anati, Munthuyo anafunsitsa za ife, ndi za abale athu, kuti, Atate wanu alipo? Kodi muli ndi mphwanu? Ndipo tinamfotokozera iye monga mwa mau amenewo: ngati tinadziwa kuti iye adzati, Idzani naye mphwanu?


Ndipo mkazi mmodzi anati, Mbuye wanga, ine ndi mkazi uyu tikhala awiri m'nyumba imodzi; ndipo ine ndinaona mwana, iye ali m'nyumbamo.