Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 43:13 - Buku Lopatulika

mutengenso mphwanu, nimunyamuke, mupitenso kwa munthu uja:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

mutengenso mphwanu, nimunyamuke, mupitenso kwa munthu uja:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtengeni mbale wanuyu, ndipo nyamukani, mupitenso kwa munthuyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mutengeninso mngʼono wanuyu ndi kubwerera kwa munthuyo msanga.

Onani mutuwo



Genesis 43:13
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Mwana wanga sadzatsikira ndi inu, chifukwa kuti mkulu wake wafa, ndipo watsala iye yekha; ngati choipa chikamgwera iye m'njira m'mene mupitamo, inu mudzatsitsira ndi chisoni imvi zanga kumanda.


nimutenge ndalama zowirikiza m'manja mwanu; ndipo ndalama zimene zinabwezedwa kukamwa kwa matumba anu mutengenso m'manja mwanu; kapena sanachite dala;


Mulungu Wamphamvuyonse adzakupatsani inu chifundo pamaso pa munthu uja, kuti akumasulireni inu mbale wanu wina ndi Benjamini. Ndipo ine, ngati ndikhala wopanda ana, ndikhalatu.