Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 43:10 - Buku Lopatulika

pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tikadapanda kuzengereza, tikadapita ndi kubwerako kaŵiri konse tsopano.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmene zililimu, tikanapanda kuchedwa, bwenzi titapita ndi kubwerako kawiri.”

Onani mutuwo



Genesis 43:10
3 Mawu Ofanana  

Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake aakazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mzinda.


Ndipo Israele atate wao anati kwa iwo, Ngati chomwecho tsopano chitani ichi: tengani zipatso za m'dziko muno m'zotengera zanu, mumtengere munthu uja mphatso, mafuta amankhwala pang'ono, ndi uchi pang'ono, zonunkhira ndi mure, ndi mfula, ndi katungurume;


Ine ndidzakhala chikole, pa manja anga mudzamfunsa: ndikapanda kumbwezera kwa inu ndi kumuimitsa pamaso panu, chifukwa chake chidzakhala pa ine masiku onse: