Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 42:31 - Buku Lopatulika

Koma ife tinati kwa iye, Tili anthu oona; sitili ozonda;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ife tinati kwa iye, Tili anthu oona; sitili ozonda;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ife tidamuuza munthuyo kuti, ‘Ndife anthu okhulupirika, osati azondi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma tinamuwuza kuti, ‘Ndife anthu woona mtima osati akazitape.

Onani mutuwo



Genesis 42:31
2 Mawu Ofanana  

Tonse tili ana aamuna a munthu mmodzi; tili oona, akapolo anu, sitili ozonda.


tili abale khumi ndi awiri, ana a atate wathu; wina palibe, ndipo lero wamng'ono ali ndi atate wathu m'dziko la Kanani.