Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 42:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Ndicho chimene ndinakunenani inu, kuti, Ndinu ozonda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Ndicho chimene ndinakunenani inu, kuti, Ndinu ozonda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yosefe adaŵayankha kuti, “Paja ndanena kale kuti ndinu azondi basi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yosefe anawawuza kuti, “Ndi momwe ndaneneramo: Inu ndinu akazitape.

Onani mutuwo



Genesis 42:14
6 Mawu Ofanana  

Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


Mubisiranji nkhope yanu, ndi kundiyesa mdani wanu?


Wandiyatsiranso mkwiyo wake, nandiyesera ngati wina wa adani ake.