Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 41:28 - Buku Lopatulika

Ichi ndi chinthu chimene ndinena kwa Farao: chimene Mulungu ati achite wasonyeza kwa Farao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ichi ndi chinthu chimene ndinena kwa Farao: chimene Mulungu ati achite wasonyeza kwa Farao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono monga momwe ndanenera, ndiye kuti Mulungu wakuuziranitu zomwe adzachite.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tsono ndi monga ndafotokozeramu kuti Mulungu wakuwuziranitu zimene adzachite.

Onani mutuwo



Genesis 41:28
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anati kwa iye, Kumasulira kwake ndi uwu: nthambi zitatu ndizo masiku atatu;


Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.


Ndipo Yosefe anati kwa Farao, Loto la Farao lili limodzi: chimene Mulungu ati achite wam'masulira Farao.


Ndipo lotolo linabwerezedwa kawiri kwa Farao, chifukwa chinthu chili chokhazikika ndi Mulungu, ndipo Mulungu afulumira kuchichita.


Umo mudaonera kuti mwala unasemedwa m'phiri popanda manja, ndi kuti udapera chitsulo, mkuwa, dongo, siliva, ndi golide; Mulungu wamkulu wadziwitsa mfumu chidzachitika m'tsogolomo; lotoli nloona, ndi kumasulira kwake kwakhazikika.