Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 41:17 - Buku Lopatulika

Ndipo Farao ananena kwa Yosefe, M'loto langa taona, ndinaima m'mphepete mwa mtsinje;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Farao ananena kwa Yosefe, M'loto langa taona, ndinaima m'mphepete mwa nyanja;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Farao adati, “Ine ndidaalota ntaimirira pamphepete pa mtsinje wa Nailo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, “Ndinalota nditayimirira mʼmphepete mwa mtsinje wa Nailo,

Onani mutuwo



Genesis 41:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.


ndipo taona, zinatuluka m'mtsinjemo ng'ombe zazikazi zisanu ndi ziwiri, zonenepa ndi za maonekedwe abwino; ndipo zinadya m'mabango;