Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 41:11 - Buku Lopatulika

ndipo tinalota loto usiku umodzi ine ndi iye; tinalota munthu yense monga mwa kumasulira kwa loto lake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo tinalota loto usiku umodzi ine ndi iye; tinalota munthu yense monga mwa kumasulira kwa loto lake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono usiku wina, aŵirife tidaalota maloto. Aliyense mwa ife anali atalota maloto ake, a tanthauzo lakelake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsiku lina tonse awiri tinalota maloto, ndipo loto lililonse linali ndi tanthauzo lake.

Onani mutuwo



Genesis 41:11
2 Mawu Ofanana  

pali munthu mu ufumu mwanu mwa iye muli mzimu wa milungu yoyera; ndipo masiku a atate wanu munapezeka mwa iye kuunika, ndi luntha, ndi nzeru, ngati nzeru ya milungu; ndipo mfumu Nebukadinezara atate wanu, inde mfumu atate wanu anamuika akhale mkulu wa alembi, openda, Ababiloni, ndi alauli;