Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 39:18 - Buku Lopatulika

ndipo panali pamene ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chovala chake kwa ine, nathawira kunja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo panali pamene ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chovala chake kwa ine, nathawira kunja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ine nditakuwa, iyeyo anasiya mwinjiro wake pafupi ndi ine, nkuthaŵira pabwalo.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma pamene ndinakuwa, iye anandisiyira mkanjo wake nathawira kunja.”

Onani mutuwo



Genesis 39:18
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena kwa iye monga mau awa, anati, Analowa kwa ine kapolo wa Chihebri uja, munabwera naye kwathu, kundipunza ine:


Ndipo panali pamene mbuyake anamva mau a mkazi wake, amene ananena kwa iye, kuti, Choterochi anandichitira ine kapolo wako; kuti iye anapsa mtima.