Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 39:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anasunga chofunda chake chikhale ndi iye kufikira atabwera kwao mbuyake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anasunga chofunda chake chikhale ndi iye kufikira atabwera kwao mbuyake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwinjirowo adangousunga m'manja kudikira mpaka bwana wa Yosefe atabwera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono mkazi wa Potifara uja anasunga mkanjowo mpaka mbuye wake wa Yosefe atabwera ku nyumba.

Onani mutuwo



Genesis 39:16
7 Mawu Ofanana  

ndipo panali pamene iye anamva kuti ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chofunda chake kwa ine nathawira kubwalo.


Ndipo ananena kwa iye monga mau awa, anati, Analowa kwa ine kapolo wa Chihebri uja, munabwera naye kwathu, kundipunza ine:


Woipa apangira chiwembu wolungama, namkukutira mano.


Woipa aunguza wolungama, nafuna kumupha.


Pakuti anthu anga apusa, sandidziwa Ine; ali ana opulukira sazindikira; ali ochenjera kuchita choipa koma kuchita chabwino sakudziwa.


Pakuti kale ifenso tinali opusa, osamvera, onyengeka, akuchitira ukapolo zilakolako ndi zokondweretsa za mitundumitundu, okhala m'dumbo ndi njiru, odanidwa, odana wina ndi mnzake.