Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 39:15 - Buku Lopatulika

ndipo panali pamene iye anamva kuti ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chofunda chake kwa ine nathawira kubwalo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo panali pamene iye anamva kuti ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chofunda chake kwa ine nathawira kubwalo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono atamva kukuwa kwangako, wasiya mwinjiro wake m'manja mwangamu nkuthaŵira pabwalo.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atandimva ndikukuwa, anandisiyira mkanjo wakewu nʼkuthawira kunja.”

Onani mutuwo



Genesis 39:15
3 Mawu Ofanana  

anaitana aamuna a m'nyumba yake, nanena ndi iwo kuti, Taonani, walowetsa kwa ife Muhebri kuti atiseke ife, analowa kwa ine kugona ndi ine, ndipo ndinafuula ndi mau aakulu:


Ndipo anasunga chofunda chake chikhale ndi iye kufikira atabwera kwao mbuyake.


Afunafuna zosalungama; kusanthula, asanthuladi mpaka kutha; chingakhale cha m'kati mwake mwa munthu, ndi mtima wozama.