Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 38:27 - Buku Lopatulika

Ndipo panali nthawi ya kubala kwake, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali nthawi ya kubala kwake, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Itakwana nthaŵi yakuti Tamara achire, m'mimba mwake munali mapasa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Tamara nthawi inamukwanira yoti abeleke, mʼmimbamo munali mapasa.

Onani mutuwo



Genesis 38:27
2 Mawu Ofanana  

Atatha masiku ake akubala, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.


Ndipo panali pamene anabala kuti mmodzi anatulutsa dzanja; ndipo namwino anatenga chingwe chofiira namanga padzanja lake, kuti, Uyu anayamba kubadwa.