Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 38:15 - Buku Lopatulika

Pamene Yuda anamuona iye, anaganizira kuti ali mkazi wadama: chifukwa iye anabisa nkhope yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene Yuda anamuona iye, anaganizira kuti ali mkazi wadama: chifukwa iye anabisa nkhope yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yuda atamuwona, adaamuyesa mkazi wadama, chifukwa anali atadziphimba kumaso.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yuda atamuona anangomuyesa mkazi wadama chabe, chifukwa anadziphimba nkhope.

Onani mutuwo



Genesis 38:15
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo anavula zovala zake zamasiye, nadzifunda ndi chofunda chake, navala nakhala pa chipata cha Enaimu, chifukwa chili panjira ya ku Timna; pakuti anaona kuti Sela anakula msinkhu, ndipo sanampatse iye kuti akhale mkazi wake.


Ndipo iye anapatukira kwa mkazi panjira, nati, Tiyetu, ndilowane nawe; chifukwa sanamdziwe kuti ndiye mpongozi wake. Ndipo anati, Kodi udzandipatsa ine chiyani kuti ulowane ndi ine.


Ndipo taona, mkaziyo anamchingamira, atavala zadama wochenjera mtima,


Kapena simudziwa kuti iye wophatikidwa ndi mkazi wachiwerewere ali thupi limodzi? Pakuti awiriwo, ati, adzakhala thupi limodzi.