Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 38:13 - Buku Lopatulika

Ndipo anamuuza Tamara, kuti, Taona, mpongozi wako akwera kunka ku Timna kuti akasenge nkhosa zake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamuuza Tamara, kuti, Taona, mpongozi wako akwera kunka ku Timna kuti akasenge nkhosa zake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wina adauza Tamara kuti, “Apongozi ako akupita ku Timna kukameta nkhosa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamara atamva kuti apongozi ake akupita ku Timna kukameta nkhosa,

Onani mutuwo



Genesis 38:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani ananka kukasenga nkhosa zake: ndipo Rakele anaba aterafi a atate wake.


Ndi Tamara mpongozi wake anambalira Perezi ndi Zera. Ana aamuna onse a Yuda ndiwo asanu.


Ndipo malire anazungulira kuyambira ku Baala kunka kumadzulo, kuphiri la Seiri, napitirira kumbali kwa phiri la Yearimu kumpoto, ndilo Kesaloni, natsikira ku Betesemesi, napitirira ku Timna;


Kaini, Gibea ndi Timna; mizinda khumi pamodzi ndi midzi yao.


Ndipo Samisoni anatsikira ku Timna, naona mkazi wa ku Timna wa ana aakazi a Afilisti.


Ndipo panali munthu ku Maoni, amene katundu wake anali ku Karimele; iyeyu anali womveka ndithu, anali nazo nkhosa zikwi zitatu, ndi mbuzi chikwi chimodzi; ndipo analikusenga nkhosa zake ku Karimele.


Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake.