Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 37:6 - Buku Lopatulika

Ndipo iye anati kwa iwo, Tamvanitu loto limene ndalota:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye anati kwa iwo, Tamvanitu loto limene ndalota:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iye adaŵauza kuti “Mverani maloto omwe ndalota.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anawawuza kuti, “Tamvani maloto amene ndinalota:

Onani mutuwo



Genesis 37:6
5 Mawu Ofanana  

Yosefe ndipo analota loto, nawafotokozera abale ake; ndipo anamuda iye koposa.


pakuti taonani, ndinalinkumanga mitolo m'munda, ndipo taonani, mtolo wanga unauka nuima chilili! Ndipo taonani, mitolo yanu inadza niuzinga kwete, niuweramira mtolo wanga.


Ndipo Yosefe anakumbukira maloto amene analota za iwo, ndipo anati kwa iwo, Ozonda inu; mwadzera kudzaona usiwa wa dziko.


Ndipo Yuda anayandikira kwa iye nati, Mfumu, kapolo wanu aneneretu m'makutu a mbuyanga, mtima wanu usapse pokwiya ndi kapolo wanu; chifukwa muli ngati Farao.


Ndipo atamuuza Yotamu, anamuka iye naimirira pamutu paphiri la Gerizimu, nakweza mau ake, nafuula, nanena nao, Mundimvere ine, eni ake a ku Sekemu inu, kuti Mulungu amvere inu.