Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 37:16 - Buku Lopatulika

Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ndikufunafuna abale anga. Chonde tandiwuzani kumene akuŵeta nkhosa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayankha, “Ndikufuna abale anga. Mungandiwuze kumene akudyetsa ziweto zawo?”

Onani mutuwo



Genesis 37:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anampeza munthu, taonani, analinkusokera m'thengo; munthuyo ndipo anamfunsa, nati, Kodi ufuna chiyani?


Munthuyo ndipo anati, Anachoka pano; pakuti ndinamva alinkuti, Timuke ku Dotani. Yosefe ndipo anatsata abale ake, nawapeza ali ku Dotani.


Ndiuze, iwe amene moyo wanga ukukonda, umaweta kuti gulu lako? Umaligonetsa kuti pakati pa usana? Pakuti ndikhalirenji ngati wosochera pambali pa magulu a anzako?


Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.