Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 36:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Ada anambalira Esau Elifazi; ndipo Basemati anabala Reuwele;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Ada anambalira Esau Elifazi; ndipo Basemati anabala Reuwele;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ada adamubalira Esau Elifazi. Basemati adabala Reuele

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ada anaberekera Esau, Elifazi; Basemati anabereka Reueli;

Onani mutuwo



Genesis 36:4
7 Mawu Ofanana  

Pamene Esau anali wa zaka makumi anai, anakwatira Yuditi mwana wamkazi wa Beeri Muhiti, ndi Basemati mwana wamkazi wa Eloni Muhiti.


ndi Basemati mwana wamkazi wa Ismaele, mlongo wake wa Nebayoti.


ndipo Oholibama anabala Yeusi, ndi Yalamu, ndi Kora; amenewa ndi ana aamuna a Esau, amene anambadwira m'dziko la Kanani.


Ana a Esau: Elifazi, Reuwele, ndi Yeusi, ndi Yalamu, ndi Kora.


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


M'mene anafika kwa Reuwele atate wao, iye anati, Mwabwera msanga bwanji lero?


Ndipo Mose anati kwa Hobabu mwana wa Reuwele Mmidiyani mpongozi wa Mose, Ife tili kuyenda kunka ku malo amene Yehova anati, Ndidzakupatsani awa; umuke nafe, tidzakuchitira zokoma; popeza Yehova wanenera Israele zokoma.