Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 34:18 - Buku Lopatulika

Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mau ameneŵa adakondweretsa kwambiri Hamori ndi mwana wake Sekemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mawu amenewa anakondweretsa Hamori ndi mwana wake Sekemu.

Onani mutuwo



Genesis 34:18
3 Mawu Ofanana  

Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.


Ndipo mnyamatayo sanachedwe kuchichita popeza anakondwera ndi mwana wake wamkazi wa Yakobo; ndipo iye anali wolemekezedwa woposa onse a pa banja la atate wake.


Ndipo mbiri yake inamveka m'nyumba ya Farao, kuti abale ake a Yosefe afika; ndipo inamkomera Farao, ndi anyamata ake.