Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 33:6 - Buku Lopatulika

Ndipo adzakazi anayandikira ndi ana ao, nawerama pansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo adzakazi anayandikira ndi ana ao, nawerama pansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adzakazi aja adadza pamodzi ndi ana ao, nagwada pansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono antchito aja anayandikira naweramitsa mitu pansi.

Onani mutuwo



Genesis 33:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anatukula maso ake nawaona akazi ndi ana; nati, Ndani awa ali ndi iwe? Ndipo iye anati, Ndiwo ana amene Mulungu anakomera mtima kumpatsa kapolo wanu.


Ndiponso Leya ndi ana ake anayandikira nawerama pansi: pambuyo pake anayandikira Yosefe ndi Rakele, nawerama pansi.