Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 33:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Esau anati, Tiyeni timuke; nditsogolera ndine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Esau anati, Tiyeni timuke; nditsogolera ndine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Esau adati, “Tiyeni tinyamuke, tizipita. Ine nditsogolako.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Esau anati, “Tiyeni tizipita; nditsagana nanu.”

Onani mutuwo



Genesis 33:12
2 Mawu Ofanana  

Landiranitu mdalitso wanga umene wafika kwa inu, pakuti Mulungu wandichitira ine zaufulu, ndipo zanganso zindikwanira. Ndipo anamkakamiza, nalandira.


Ndipo anati kwa iye, Mbuyanga adziwa kuti ana ali anthete, ndipo nkhosa ndi zoweta ndili nazo zilinkuyamwitsa: ndipo akathamangitsa tsiku limodzi zoweta zonse zidzafa.