Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 31:9 - Buku Lopatulika

Chomwecho Mulungu anazichotsa zoweta za atate wanu, nandipatsa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chomwecho Mulungu anazichotsa zoweta za atate wanu, nandipatsa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu watenga zoŵeta zonse kwa bambo wanu, wapatsa ine.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Motero Mulungu walanda abambo anu ziweto zawo ndi kundipatsa.

Onani mutuwo



Genesis 31:9
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ziweto zinatenga mabere patsogolo pa nthyolezo, ndipo zoweta zinabala zamipyololomipyololo, ndi mathothomathotho, ndi zamawangamawanga.


Ndipo anamva mau a ana ake a Labani kuti, Yakobo watenga zonse za atate wathu; m'zinthu zinali za atate wathu wapeza iye chuma ichi chonse.


Ndipo panali potenga mabere ziwetozo, ine ndinatukula maso anga, ndipo ndinapenya m'kulota, taonani, atonde okwera ziweto anali amipyololomipyololo, amathothomathotho, ndi amawangamawanga.


Chifukwa kuti chuma chonse Mulungu anachichotsa kwa atate wathu ndi chathu ndi cha ana athu; tsono, zonse wakunenera iwe Mulungu, uchite.


mbuzi zazikazi mazana awiri, atonde makumi awiri, nkhosa zazikazi mazana awiri, ndi zazimuna makumi awiri,


Pakuti zamoyo zonse zakuthengo ndi zanga, ndi ng'ombe za pa mapiri zikwi.


Wabwino asiyira zidzukulu zake cholowa chabwino; koma wochimwa angosungira wolungama chuma chake.


Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino?