Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 31:6 - Buku Lopatulika

Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nonse aŵirinu mukudziŵa bwino kuti ndidagwira ntchito kwa bambo wanu ndi mphamvu zanga zonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mukudziwa kuti ndagwirira ntchito abambo anu ndi mphamvu zanga zonse,

Onani mutuwo



Genesis 31:6
8 Mawu Ofanana  

Undipatse ine akazi anga ndi ana anga chifukwa cha iwowa ndakutumikira iwe, ndimuke: chifukwa udziwa iwe ntchito imene ndinakugwirira iwe.


Ndipo iye anati kwa Labani, Udziwa iwe chomwe ndakutumikira iwe ndi chomwe zachita zoweta zako ndi ine.


Ndipo atate wanu wandinyenga ine, nasinthanitsa malipiro anga kakhumi; koma Mulungu sanamlole iye andichitire ine choipa.


Anyamata inu, gonjerani ambuye anu ndi kuopa konse, osati abwino ndi aulere okha, komanso aukali.