Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 31:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Yakobo anatumiza naitana Rakele ndi Leya adze kubusa ku zoweta zake,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yakobo anatumiza naitana Rakele ndi Leya adze kubusa ku zoweta zake,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yakobe adatumiza mau kwa Rakele ndi kwa Leya kuti akakumane naye kubusa kumene kunali zoŵeta zake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Yakobo anatumiza mawu kukayitana Rakele ndi Leya kuti abwere ku busa kumene ankaweta ziweto zake.

Onani mutuwo



Genesis 31:4
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anali ndi ana aakazi awiri, dzina la wamkulu ndi Leya, dzina la wamng'ono ndi Rakele.


Ndipo Yehova anati kwa Yakobo, Bwera ku dziko la atate wako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakhala ndi iwe.


ndipo anati kwa iwo, Ndiona ine nkhope ya atate wanu kuti siindionekere ine monga kale; koma Mulungu wa atate wanga anali ndi ine.