Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 30:34 - Buku Lopatulika

Ndipo Labani anati, Taona, kukhale monga mau ako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Labani anati, Taona, kukhale monga mau ako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Labani adavomera, adati, “Chabwino. Tichite monga waneneramo.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Labani anati, “Ndavomera, zikhale monga mmene wayankhuliramu.”

Onani mutuwo



Genesis 30:34
6 Mawu Ofanana  

Chotero chilungamo changa chidzandivomereza m'tsogolo pamene udzandifika chifukwa cha malipiro amene ali patsogolo pako: iliyonse yosakhala yamathothomathotho ndi yamawangamawanga ya mbuzi, ndi iliyonse ya nkhosa yosakhala yakuda, ikapezedwa ndi ine, udzaiyesa yakuba.


Tsiku lomwelo Labani anachotsa atonde amene anali amipyololomipyololo ndi amathothomathotho, ndi mbuzi zazikazi zinali zamawangamawanga ndi zamathothomathotho zonse zinali zoyera pang'ono, ndi zakuda zonse za nkhosa, napatsa m'dzanja la ana ake aamuna.


Pamenepo Balamu anati kwa bulu, Chifukwa wandipeputsa; mukadakhala lupanga m'dzanja langa tsopano, ndikadakupha iwe.


Ndipo ndifuna inu nonse mulankhule malilime, koma makamaka kuti mukanenere; ndipo wakunenera aposa wakulankhula malilime, akapanda kumasulira, kuti Mpingo ukalandire chomangirira.


Koma mwenzi anthu onse akadakhala monga momwe ndili ine ndekha. Koma munthu yense ali nayo mphatso yake ya iye yekha kwa Mulungu, wina chakuti, wina chakuti.


Mwenzi atadzidula, iwo akugwedezetsani inu.