Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 30:21 - Buku Lopatulika

Pambuyo pake ndipo anabala mwana wamkazi, namutcha dzina lake Dina.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pambuyo pake ndipo anabala mwana wamkazi, namutcha dzina lake Dina.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake adabala mwana wamkazi, namutcha Dina.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Patapita nthawi Leya anabereka mwana wamkazi ndipo anamutcha Dina.

Onani mutuwo



Genesis 30:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Mulungu anandipatsa ine mphatso yabwino; tsopano mwamuna wanga adzakhala ndi ine, chifukwa ndambalira iye ana aamuna asanu ndi mmodzi; ndipo anamutcha dzina lake Zebuloni.


Ndipo Mulungu anakumbukira Rakele, ndipo Mulungu anamvera iye, natsegula m'mimba mwake.


Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wake ndi lupanga, natulutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nachoka naye.


Amenewo ndi ana aamuna a Leya, amene anambalira Yakobo ku Padanaramu, pamodzi ndi mwana wamkazi wake Dina; ana aamuna ndi aakazi onse ndiwo anthu makumi atatu kudza atatu.