Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 30:10 - Buku Lopatulika

Ndipo Zilipa mdzakazi wake wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Zilipa mdzakazi wake wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Zilipa adabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zilipa, wantchito wa Leya, anaberekera Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo



Genesis 30:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi.


Pamene Leya anaona kuti analeka kubala, anatenga Zilipa mdzakazi wake, nampatsa iye kwa Yakobo kuti akhale mkazi wake.


ndipo ana aamuna a Zilipa mdzakazi wake wa Leya: ndiwo Gadi ndi Asere: amenewo ndi ana aamuna a Yakobo amene anabala iye mu Padanaramu.


Ndi kumalire a Zebuloni, kuyambira kumbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Gadi, limodzi.


A ana a Gadi, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Koma ana a Rubeni ndi ana Gadi anali nazo zoweta zambirimbiri; ndipo anapenyerera dziko la Yazere, ndi dziko la Giliyadi, ndipo taonani, malowo ndiwo malo a zoweta.