Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:26 - Buku Lopatulika

Ndipo Isaki atate wake anati kwa iye, Senderatu, undimpsompsone mwana wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Isaki atate wake anati kwa iye, Senderatu, undimpsompsone mwana wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono bambo wakeyo adati, “Bwera pafupi, udzandimpsompsone, mwana wanga.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Isake anati kwa Yakobo, “Bwera kuno mwana wanga undipsompsone.”

Onani mutuwo



Genesis 27:26
6 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Usendere nayo kwa ine, ndidye nyama ya mwana wanga, kuti moyo wanga ukudalitse iwe. Ndipo anasendera nayo kwa iye, nadya iye; ndipo anamtengera vinyo, namwa iye.


Ndipo anasendera nampsompsona; ndipo anamva kununkhira kwa zovala zake, namdalitsa, nati, Taona, kununkhira kwa mwana wanga, kufanana ndi kununkhira kwa munda anaudalitsa Yehova;


Ndipo Yakobo anampsompsona Rakele nakweza mau ake, nalira.


Chomwecho Yowabu anadza kwa mfumu namuuza; ndipo pamene iye adaitana Abisalomu, iye anadza kwa mfumu naweramira nkhope yake pansi pamaso pa mfumu; ndipo mfumu inampsompsona Abisalomu.


Mnyamatayo andipsompsonetse ndi m'kamwa mwake; pakuti chikondi chako chiposa vinyo.


Ndipo pomwepo anadza kwa Yesu, nati, Tikuoneni, Rabi; nampsompsonetsa.