Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:17 - Buku Lopatulika

ndipo anapereka m'dzanja la mwana wake Yakobo chakudya chokoleracho, ndi mikate imene anaipanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anapereka m'dzanja la mwana wake Yakobo chakudya chokoleracho, ndi mikate imene anaipanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo adatenga buledi ndi chakudya chokonza bwino chija, napatsira Yakobe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka, anamupatsa Yakobo chakudya chokoma chija chimene anaphika pamodzi ndi buledi.

Onani mutuwo



Genesis 27:17
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuka nakatenga nadza nato kwa amake; amake ndipo anakonza chakudya chokolera chonga chimene anachikonda atate wake.


ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;


Ndipo iye analowa kwa atate wake, nati, Atate wanga; iye anati, Ndine pano; ndani iwe mwana wanga?


nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.