Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:35 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anapweteka mtima wa Isaki ndi wa Rebeka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo iwo anapweteka mtima wa Isaki ndi wa Rebeka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Onseŵa adapezetsa Isaki ndi Rebeka mavuto aakulu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Akazi awiriwa anasandutsa Isake ndi Rebeka kukhala ndi moyo wa madandawulo nthawi zonse.

Onani mutuwo



Genesis 26:35
5 Mawu Ofanana  

ndipo ndidzakulumbiritsa iwe pa Yehova, Mulungu wa Kumwamba, ndi Mulungu wa dziko lapansi, kuti usadzamtengere mwana wanga mkazi wa kwa ana aakazi a Akananiwo, amene ndikhala pakati pao.


Ndipo anati Rebeka kwa Isaki, Ndalema moyo wanga chifukwa cha ana aakazi a Ahiti, akatenga Yakobo mkazi wa ana aakazi a Ahiti, onga ana aakazi a m'dziko lino, moyo wanga udzandikhalira ine bwanji?


ndipo Esau anaona kuti ana aakazi a Kanani sanakondweretse Isaki atate wake:


kuti ana aamuna a Mulungu anayang'ana ana aakazi a anthu, kuti iwo anali okongola; ndipo anadzitengera okha akazi onse amene anawasankha.