Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:21 - Buku Lopatulika

Ndipo anakumbanso chitsime china, ndipo anakangana nachonso; natcha dzina lake Sitina.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anakumbanso chitsime china, ndipo anakangana nachonso; natcha dzina lake Sitina.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Antchito a Isaki aja adakumba chitsime china, ndipo padaukanso mkangano wina pa za chitsime chimenecho. Motero adachitcha Chidani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka iwo anakumba chitsime china, koma anakangananso chifukwa cha chitsimecho. Choncho anachitcha dzina lakuti Chidani.

Onani mutuwo



Genesis 26:21
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.


Ndipo abusa a Gerari anakangana ndi abusa a Isaki kuti, Madzi ndi athu; ndipo anatcha dzina la chitsimecho Eseke: chifukwa anakangana naye.


Ndipo anachoka kumeneko nakumba chitsime china; koma sanakangane nacho chimenecho; ndipo anatcha dzina lake Rehoboti; ndipo anati, Chifukwa kuti tsopano Yehova anatipatsa ife malo, ndipo tidzabalana m'dziko muno.


Ndipo pokhala mfumu Ahasuwero, poyambira ufumu wake, analembera chowaneneza okhala mu Yuda ndi mu Yerusalemu.