Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 25:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Abrahamu anatenga mkazi wina dzina lake Ketura.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abrahamu anatenga mkazi wina dzina lake Ketura.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abrahamu adakwatiranso mkazi wina dzina lake Ketura.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abrahamu anakwatira mkazi wina dzina lake Ketura.

Onani mutuwo



Genesis 25:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anamlowetsa mkaziyo m'hema wa amake Sara, namtenga Rebeka, nakhala iye mkazi wake; ndipo anamkonda iye; ndipo Isaki anatonthozedwa mtima atafa amake.


Ndipo anambalira iye Zimirani ndi Yokisani ndi Medani, ndi Midiyani, ndi Isibaki, ndi Suwa.


Ndipo Isaki anamuitana Yakobo, namdalitsa iye, namuuza iye, nati kwa iye, Usatenge mkazi wa ana aakazi a Kanani.