Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 24:66 - Buku Lopatulika

Mnyamatayo ndipo anamuuza Isaki zonse anazichita.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mnyamatayo ndipo anamuuza Isaki zonse anazichita.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wantchitoyo adamufotokozera Isaki zonse zimene zidaachitika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono wantchito uja anawuza Isake zonse zimene anazichita.

Onani mutuwo



Genesis 24:66
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa mnyamata, Munthuyo ndani amene ayenda m'munda kukomana ndi ife? Mnyamatayo ndipo anati, Uyo ndi mbuyanga: chifukwa chake namwali anatenga chophimba chake nadziphimba.


Ndipo Isaki anamlowetsa mkaziyo m'hema wa amake Sara, namtenga Rebeka, nakhala iye mkazi wake; ndipo anamkonda iye; ndipo Isaki anatonthozedwa mtima atafa amake.


Ndipo atumwi anasonkhana kwa Yesu; namuuza zilizonse adazichita, ndi zonse adaziphunzitsa.