Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 24:57 - Buku Lopatulika

Ndipo anati iwo, Tidzamuitana namwaliyo, tidzamfunsa pakamwa pake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati iwo, Tidzamuitana namwaliyo, tidzamfunsa pakamwa pake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo iwowo adayankha kuti, “Tiyeni timuitane namwaliyo, kuti timve zimene iyeyo anene.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iwo anati, “Bwanji timuyitane mtsikanayo ndipo timufunse ngati afuna kupita nanu panopa.”

Onani mutuwo



Genesis 24:57
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati kwa iwo, Musandichedwetse ine, pakuti Yehova wandiyendetsa bwino m'njira yanga: mundilole ine ndinke kwa mbuyanga.


Ndipo anamuitana Rebeka nati kwa iye, Kodi udzanka pamodzi ndi munthuyo? Ndipo anati, Ndidzanka.


Cholamulira Yehova za ana aakazi a Zelofehadi ndi ichi, kuti, Akwatibwe nao amene afuna eni ake; komatu akwatibwe nao a banja la fuko la makolo ao okhaokha.