Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 24:39 - Buku Lopatulika

Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo ine ndidamuyankha mbuyanga kuti, ‘Nanga zidzatani ngati mkaziyo adzakana kubwera nane kuno?’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ndipo ine ndinati kwa mbuye wanga, ‘Nanga mkaziyo akakapanda kubwera nane pamodzi?’

Onani mutuwo



Genesis 24:39
2 Mawu Ofanana  

koma udzanke kunyumba ya atate wanga, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga mkazi.


Ndipo anati kwa iye mnyamatayo, Kapena sadzafuna mkaziyo kunditsata ine ku dziko lino: kodi ndikambwezerenso mwana wanu ku dziko komwe mwachokera inu?