Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 24:25 - Buku Lopatulika

Natinso kwa iye, Tili nao udzu ndi zakudya zambiri ndi malo ogona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Natinso kwa iye, Tili nao udzu ndi zakudya zambiri ndi malo ogona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Chakudya chodyetsa nyamazi chiliko kwathu, ndipo malo oti inu mugoneko aliponso.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anapitiriza kunena kuti, “Chakudya chodyetsa nyamazi chilipo kwathu ndipo malo woti mugone aliponso.”

Onani mutuwo



Genesis 24:25
8 Mawu Ofanana  

Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Ine ndine mwana wa Betuele mwana wamwamuna wa Milika, amene anambalira Nahori.


Munthuyo ndipo anawerama mutu namyamika Yehova.


Munthuyo ndipo analowa m'nyumba, namasula ngamira, napatsa ngamira udzu ndi chakudya, ndi madzi akusamba mapazi ake ndi mapazi a iwo amene anali naye.


Ndipo pamene wina wa iwo anamasula thumba lake kuti adyetse bulu wake pachigono, anapeza ndalama zake; taonani, zinali kukamwa kwa thumba lake.


Koma mfulu aganizira zaufulu, nakhazikika m'zaufulu zomwe.


mucherezane wina ndi mnzake, osadandaula: