Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 23:5 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthuwo adamuyankha kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu a ku Hiti aja anamuyankha Abrahamu kuti,

Onani mutuwo



Genesis 23:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wake, ndi Heti,


Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,


Ine ndine mlendo wakukhala ndi inu: mundipatse ndikhale ndi manda pamodzi ndi inu, kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso.


Mutimvere ife mfumu, ndinu kalonga wamkulu pakati pa ife; muike wakufa wanu m'manda mwathu mosankhika: palibe munthu yense wa ife adzakaniza manda ake, kuti muike wakufa wanu.


Ndi Kanani anabala Sidoni mwana wake woyamba, ndi Heti,


Koma aika waumphawi pamsanje posazunzika, nampatsa mabanja ngati gulu la nkhosa.