Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 23:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Efuroni anamyankha Abrahamu, nati kwa iye,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Efuroni anamyankha Abrahamu, nati kwa iye,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Efuroni adayankha kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Efroni anamuyankha Abrahamu nati,

Onani mutuwo



Genesis 23:14
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena kwa Efuroni alinkumva anthu a m'dzikomo, kuti, Koma ngati ufuna, undimveretu ine: ndidzakupatsa iwe mtengo wake wa munda; uulandire kwa ine, ndipo ndidzaika wakufa wanga m'menemo.


Mfumu, mundimvere ine; kadziko ka mtengo wake wa masekeli a siliva mazana anai, ndiko chiyani pakati pa ine ndi inu? Ikani wakufa wanu.