Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 21:24 - Buku Lopatulika

Ndipo Abrahamu anati, Ine ndidzalumbira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abrahamu anati, Ine ndidzalumbira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abrahamu adati, “Ndikulumbira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abrahamu anati, “Ine ndikulumbira.”

Onani mutuwo



Genesis 21:24
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza wina amene anapulumuka namuuza Abramu Muhebri; ndipo iye analinkukhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure Mwamori, mkulu wake wa Esikolo, ndi mkulu wake wa Anere; amenewo ndiwo opangana naye Abramu.


tsopano iwe undilumbirire ine pano pa Mulungu kuti sudzandinyenga ine, kapena mwana wanga, kapena mdzukulu wanga: koma monga ufulu ndakuchitira iwe udzandichitire ine, ndi dziko lomwe wakhalamo, ngati mlendo.


Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.


Ndipo anati, Undilumbirire ine; namlumbirira iye. Ndipo Israele anawerama kumutu kwa kama.


Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.


Pakuti anthu amalumbira pa wamkulu; ndipo m'chitsutsano chao chilichonse lumbiro litsiriza kutsimikiza.