Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 20:10 - Buku Lopatulika

Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Unaona chiyani iwe kuti wachita ichi?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Unaona chiyani iwe kuti wachita ichi?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”

Onani mutuwo



Genesis 20:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Farao anaitana Abramu, nati, Nanga nchiyani ichi wandichitira ine? Chifukwa chanji sunandiuze ine kuti ndiye mkazi wako?


Ndipo Abrahamu anati, Chifukwa ndinati, Pompano palibe ndithu kumuopa Mulungu, ndipo adzandipha ine chifukwa cha mkazi wanga.


Ndipo Abimeleki anaitana Abrahamu, nati kwa iye, Watichitira ife chiyani iwe? Ndakuchimwiranji iwe kuti waufikitsa pa ine ndi pa ufumu wanga uchimo waukulu? Wandichitira ine zosayenera kuzichita.