Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 19:26 - Buku Lopatulika

Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma mkazi wa Loti adaacheukira m'mbuyo, ndiye pomwepo adasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.

Onani mutuwo



Genesis 19:26
5 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.


Wobwerera m'mbuyo m'mtima adzakhuta njira yake; koma munthu wabwino adzakhuta za mwa iye yekha.


mbale zofukizazo za iwo amene adachimwira moyo waowao, ndipo azisule zaphanthiphanthi, zikhale chivundikiro cha guwa la nsembe; popeza anabwera nazo pamaso pa Yehova, chifukwa chake zikhala zopatulika; ndipo zidzakhala chizindikiro kwa ana a Israele.


Koma wolungama wangayo adzakhala ndi moyo wochokera m'chikhulupiriro: Ndipo ngati abwerera, moyo wanga ulibe kukondwera mwa iye.