Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 19:23 - Buku Lopatulika

Ndipo dzuwa lidakwera padziko pamene Loti anafika ku Zowari.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo dzuwa lidakwera pa dziko pamene Loti anafika ku Zowari.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene dzuŵa linkatuluka, Loti nkuti atafika kale ku Zowari.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Loti amafika ku Zowari, nʼkuti dzuwa litatuluka.

Onani mutuwo



Genesis 19:23
3 Mawu Ofanana  

Fulumira, thawira kumeneko; pakuti sindithai kuchita kanthu usadafike kumeneko. Chifukwa chake anatcha dzina la mzindawo Zowari.


Ndipo Yehova anavumbitsa pa Sodomu ndi pa Gomora miyala ya sulufure ndi moto kutuluka kwa Mulungu kumwamba;


Ndipo kudamchera iye pamene anaoloka pa Penuwele, ndipo iye anatsimphina ndi ntchafu yake.