Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 19:18 - Buku Lopatulika

Ndipo Loti anati kwa iwo, Iaitu, mfumu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Loti anati kwa iwo, Iaitu, mfumu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Loti adamuyankha kuti, “Iyai mbuyanga musatero.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Loti anawawuza kuti, “Ayi, ambuye anga chonde musatero!

Onani mutuwo



Genesis 19:18
8 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.


taonanitu, kapolo wanu anapeza ufulu pamaso panu, ndipo munakuza chifundo chanu, chimene munandichitira ine, pakupulumutsa moyo wanga; ine sindikhoza kuthawira kuphiri kuti chingandipeze ine choipacho ndingafe;


Ndipo iye anati Ndileke ndimuke, chifukwa kulinkucha. Ndipo Yakobo anati, Sindidzakuleka iwe kuti umuke, ukapanda kundidalitsa ine.


Atero Yehova Woyera wa Israele ndi Mlengi wake, Ndifunse Ine za zinthu zimene zilinkudza; za ana anga aamuna, ndi za ntchito ya manja anga, ndilamulireni Ine.


Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadye ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa.


Ndipo Ananiya anayankha nati, Ambuye, ndamva ndi ambiri za munthu uyu, kuti anachitiradi choipa oyera mtima anu mu Yerusalemu;